Temwah – Malawi

Temwah Malawi

Temwah – Malawi Lyrics

Artist: Temwah
Song: Malawi

M-A Lawi-Lawi
Malawi, Ndati-Ndati
Timadya nkhwani wa mati-mati
Kuphika thobwa la khati-khati

Ku Malawi, Manganje
Yamba kuvina usathawe
Ku Nsanje, mwa chaje
Chi Sena chiyankhulo chake

Tikafuna Utaka, sitichita kusaka
Lake Malawi is blessed with some beautiful fish (Beautiful fish)
Tikafuna Utaka, Abale sitichita kusaka
Lake Malawi is blessed with some beautiful fish (Beautiful fish)

Chikhalidwe’chi nchakwathu
Chiyankhulo’chi nchakwathu
Mavalidwewa ngakwathu
Mavinidwewa ngakwathu

Chiyankhulidwe nchakwathu
Mayankhulidwe ngakwathu
Ngakwathu…
Kukacha mamawa

Timapita kumunda, Kukalima
Zolima Zija ha
Sitisiyila pompo, Kupalira
Nanga Udya bwanji osalima?

Ulemera bwanji osavepa?
Nsanje, mtima osadekha
Kukhala ndi anthu nzosatheka
Tisanimizane makosana

Hard work pays, never fails a dream
Galu Okuda suzamuona
Alendo nawo sasowa chotola
Anthu ake ngasangala

Timalandira anthu mwansagala
Uku tikuchezelana nthabwala
Dziko lathu la uchi ndi mkaka
Chikhalidwe’chi nchakwathu

Chiyankhulo’chi nchakwathu
Mavalidwewa ngakwathu
Mavinidwewa ngakwathu
Chiyankhulidwe nchakwathu

Mayankhulidwе ngakwathu
Ngakwathu…
Chikhalidwe’chi nchakwathu
Chiyankhulo’chi nchakwathu

Mavalidwewa ngakwathu
Mavinidwewa ngakwathu
Chiyankhulidwе nchakwathu
Mayankhulidwe ngakwathu

Ngakwathu…
Find more lyrics at https://dcslyrics.com

You can purchase their music thru
DCSLyrics.com Amazon Music    DCSLyrics.com Apple Music
Disclosure: As an Amazon Associate and an Apple Partner, we earn from qualifying purchases

Malawi Lyrics – English Translation

A – Awake – Lawi
Malawi, I say-say
We eat a mid-di-site
Baking up in the walls of the screen-leprosy

In Malawi, Manganza
First dancing don’t run away
To envy, by charges
Chi not the language

When we want to work, we don’t search
Lake Malawi Is Blockd With’s Some Beautiful Fish (Beaautiful Fish)
When we want Usaka, the brothers don’t search
Lake Malawi Is Blockd With’s Some Beautiful Fish (Beaautiful Fish)

This Clear Island
This language is home
Dressing
The dances are missions

Speech is my own
A Sudden speaker
12
To let the morning

We go to the field, to plow
Zikoa ha
We do not insist on it, weeping
So how do you eat not to farm?

How to wear do not
Jealousy, Imperitous heart
Being with people are impossible
Try to match the selections

HARD WORK PAYS, Never Fails of DREAMS
The black dog does not see
Guests with no longer missing
His people are happy

We receive people in a bad
This is a joke
Our world’s honey and milk
This Clear Island

This language is home
Dressing
The dances are missions
Speech is my own

The Great Communion
12
This Clear Island
This language is home

Dressing
The dances are missions
N’T Fenching
A Sudden speaker

12
Find more lyrics at https://dcslyrics.com

Temwah Lyrics – Malawi

Please support our site by sharing it.
And please follow our site to get the latest lyrics for all your favourite songs.

Please support the artist and us by purchasing your favourite music thru our Amazon Music and Apple Music links 🙂

You can purchase their music thru
DCSLyrics.com Amazon Music    DCSLyrics.com Apple Music
Disclosure: As an Amazon Associate and an Apple Partner, we earn from qualifying purchases

Release Year: 2017