
SevenOmore – My Malawi Lyrics
Artist: SevenOmore
Song: My Malawi
Amangolira (Mayi Malawi)
Walira (Mayi Malawi)
Amangorila (Mayi Malawi)
Walira (Mayi Malawi)
Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ana anga inu
Ana anga inu
Amangoti Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ndikuvutika ndikuzuzika inu mulipo
Taonani ndinakupatsani kamoyo kabwino, kokongola
Inu taonani ndinakupatsani tiana tabwino, tokongola
Koma nokha nokha
Mukumaphana
Mukumalimbana
Mukumatembelerana
Mukumaponderezana
Simukukondana
Mukumasalana
Mukumatamba
Chosecho manune (Mayi wanu ine) kachitenje ndikamozi
Kamalaya ndikamozi
Ka burangete ndikamozi (Yah)
Amangolira (Mayi Malawi)
Walira (Mai Malawi)
Amangorila (Mayi Malawi)
Walira (Mayi Malawi)
Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ana anga inu
Ana anga inu
Amangoti Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ndikuvutika ndikuzuzika inu mulipo
Chumachi ndi changa
Magalimotowa ndianga
Mumapangira miyala yanga
Mafuta ndi anga
Ngakhare magetsi ndi anga
Zimapangidwa ndimadzi anga
Koma nokha nokha mukudzilengela matenda
Machilitso ndikumagulitsana
Ndinu akhwidzi
Muli ndizisisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sih
Muli ndizisisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sih
Amangolira
Amangolira (Mayi Malawi)
Walira (Mayi Malawi)
Amangorila (Mayi Malawi)
Walira (Mayi Malawi)
Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ana anga inu
Ana anga inu
Amangoti Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ndikuvutika ndikuzuzika inu mulipo
Amandiseka azimayi azanga tikakumana kumagulu
Mai Malawi mumakhala ngati simunaberekepo inu
Amandidabwa azimai azanga tikakumana kumaguru
Mai Malawi mumakhala ngati simumamuopa mulungu
Komatu ife timakusilirani
Muli ndikanyanja kabwino
Muli ndimitsinje yabwino
Muli ndikanyengo kabwino
Muli ndika thaka kabwino
Muli ndizinyama zabwino
Muli ndimapiri abwino
Ana anu ndiopirila bwino
Nkona ndikakhala ndimagwada pansi
Kumpembedza Namalenga m’mwamba
Chonde mbuye dziko musalilange Mulange ine monga kholo lawo
Oh my God
Yah-yah, yah
(Mayi Malawi)
(Mayi Malawi)
Yaachina Seven adah
(Mayi Malawi)
(Mayi Malawi)
(Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
(Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Find more lyrics at https://dcslyrics.com


Disclosure: As an Amazon Associate and an Apple Partner, we earn from qualifying purchases
SevenOmore – Palowa Njoka
SevenOmore – Pogona
My Malawi Lyrics – English Translation
They just cry (Mother Malawi)
He has cried (Mother Malawi)
Mayangorila (Mrs.ks)
He has cried (Mother Malawi)
They just say (No – no, no-nothing – no-nothing – no)
My kids you
My kids you
They just say (no-no – no, no-no-nothing – no)
I’m going to suffer and be in touch you exist
Behold, I gave you a beautiful, beautiful person
You look forward to you good, beautiful little children
But alone alone
In the same time
You’re going to fight
You’re cubeing
You’re going oppression
You are not in love
You are sighing
You’re taping
Chosecho Manume (your mother, I) to make a mammal
Maya
Buratetete Inso (Yah)
They just cry (Mother Malawi)
She’s cried (Mai · iti)
Mayangorila (Mrs.ks)
He has cried (Mother Malawi)
They just say (No – no, no-nothing – no-nothing – no)
My kids you
My kids you
They just say (no-no – no, no-no-nothing – no)
I’m going to suffer and be in touch you exist
This item is mine
The cars are going to build
You make my stones
Oil is mine
And the lights and mine
It is made of my water
But only yourself you create infectious diseases
Healing and sell each other
You’re a native
Gide, Sisi, SIS, SISi, SISI, SIS, SIH
Gide, Sisi, SIS, SISi, SISI, SIS, SIH
They only crush
They just cry (Mother Malawi)
He has cried (Mother Malawi)
Mayangorila (Mrs.ks)
He has cried (Mother Malawi)
They just say (No – no, no-nothing – no-nothing – no)
My kids you
My kids you
They just say (no-no – no, no-no-nothing – no)
I’m going to suffer and be in touch you exist
She makes me laugh at my mothers when we meet in groups
Mai Malawi is like if you haven’t bounce you
They are surprised to Azimai a shopping when we meet buildings
Machi’na · its are like you never fearing God
Yet, we admire you
You are by a better sea
You have the best rivers
You’re a good ease
You are when you are nice
You have good animals
You have a good mountains
Your Children are Completely Fight
A candidate when I’m kneeling down
Worship the Creator of heaven
Please do not master the world punish punish me as a parent
Oh my god
Yah-yah, yah
(Mother Malawi)
(Mother Malawi)
Seven of achina adah
(Mother Malawi)
(Mother Malawi)
(No-no-no-no, no-no-no-no-no)
(No-no-no-no, no-no-no-no-no)
Find more lyrics at https://dcslyrics.com
SevenOmore Lyrics – My Malawi
Please support our site by sharing it.
And please follow our site to get the latest lyrics for all your favourite songs.
Please support the artist and us by purchasing your favourite music thru our Amazon Music and Apple Music links 🙂


Disclosure: As an Amazon Associate and an Apple Partner, we earn from qualifying purchases
From the album:
My Malawi
Release Year: 2022