SevenOmore – My Malawi

SevenOmore My Malawi

SevenOmore – My Malawi Lyrics

Artist: SevenOmore
Song: My Malawi

Amangolira (Mayi Malawi)
Walira (Mayi Malawi)
Amangorila (Mayi Malawi)
Walira (Mayi Malawi)

Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ana anga inu
Ana anga inu
Amangoti Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)

Ndikuvutika ndikuzuzika inu mulipo
Taonani ndinakupatsani kamoyo kabwino, kokongola
Inu taonani ndinakupatsani tiana tabwino, tokongola
Koma nokha nokha

Mukumaphana
Mukumalimbana
Mukumatembelerana
Mukumaponderezana

Simukukondana
Mukumasalana
Mukumatamba
Chosecho manune (Mayi wanu ine) kachitenje ndikamozi

Kamalaya ndikamozi
Ka burangete ndikamozi (Yah)
Amangolira (Mayi Malawi)
Walira (Mai Malawi)

Amangorila (Mayi Malawi)
Walira (Mayi Malawi)
Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ana anga inu

Ana anga inu
Amangoti Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ndikuvutika ndikuzuzika inu mulipo
Chumachi ndi changa

Magalimotowa ndianga
Mumapangira miyala yanga
Mafuta ndi anga
Ngakhare magetsi ndi anga

Zimapangidwa ndimadzi anga
Koma nokha nokha mukudzilengela matenda
Machilitso ndikumagulitsana
Ndinu akhwidzi

Muli ndizisisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sih
Muli ndizisisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sisi, sih
Amangolira
Amangolira (Mayi Malawi)

Walira (Mayi Malawi)
Amangorila (Mayi Malawi)
Walira (Mayi Malawi)
Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)

Ana anga inu
Ana anga inu
Amangoti Amangoti (Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Ndikuvutika ndikuzuzika inu mulipo

Amandiseka azimayi azanga tikakumana kumagulu
Mai Malawi mumakhala ngati simunaberekepo inu
Amandidabwa azimai azanga tikakumana kumaguru
Mai Malawi mumakhala ngati simumamuopa mulungu

Komatu ife timakusilirani
Muli ndikanyanja kabwino
Muli ndimitsinje yabwino
Muli ndikanyengo kabwino

Muli ndika thaka kabwino
Muli ndizinyama zabwino
Muli ndimapiri abwino
Ana anu ndiopirila bwino

Nkona ndikakhala ndimagwada pansi
Kumpembedza Namalenga m’mwamba
Chonde mbuye dziko musalilange Mulange ine monga kholo lawo
Oh my God

Yah-yah, yah
(Mayi Malawi)
(Mayi Malawi)
Yaachina Seven adah

(Mayi Malawi)
(Mayi Malawi)
(Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
(Ayi-ayi-ayi-ayi, ayi-ayi-ayi-ayi-ayi)
Find more lyrics at https://dcslyrics.com

You can purchase their music thru
DCSLyrics.com Amazon Music    DCSLyrics.com Apple Music
Disclosure: As an Amazon Associate and an Apple Partner, we earn from qualifying purchases

My Malawi Lyrics – English Translation

They just cry (Mother Malawi)
He has cried (Mother Malawi)
Mayangorila (Mrs.ks)
He has cried (Mother Malawi)

They just say (No – no, no-nothing – no-nothing – no)
My kids you
My kids you
They just say (no-no – no, no-no-nothing – no)

I’m going to suffer and be in touch you exist
Behold, I gave you a beautiful, beautiful person
You look forward to you good, beautiful little children
But alone alone

In the same time
You’re going to fight
You’re cubeing
You’re going oppression

You are not in love
You are sighing
You’re taping
Chosecho Manume (your mother, I) to make a mammal

Maya
Buratetete Inso (Yah)
They just cry (Mother Malawi)
She’s cried (Mai · iti)

Mayangorila (Mrs.ks)
He has cried (Mother Malawi)
They just say (No – no, no-nothing – no-nothing – no)
My kids you

My kids you
They just say (no-no – no, no-no-nothing – no)
I’m going to suffer and be in touch you exist
This item is mine

The cars are going to build
You make my stones
Oil is mine
And the lights and mine

It is made of my water
But only yourself you create infectious diseases
Healing and sell each other
You’re a native

Gide, Sisi, SIS, SISi, SISI, SIS, SIH
Gide, Sisi, SIS, SISi, SISI, SIS, SIH
They only crush
They just cry (Mother Malawi)

He has cried (Mother Malawi)
Mayangorila (Mrs.ks)
He has cried (Mother Malawi)
They just say (No – no, no-nothing – no-nothing – no)

My kids you
My kids you
They just say (no-no – no, no-no-nothing – no)
I’m going to suffer and be in touch you exist

She makes me laugh at my mothers when we meet in groups
Mai Malawi is like if you haven’t bounce you
They are surprised to Azimai a shopping when we meet buildings
Machi’na · its are like you never fearing God

Yet, we admire you
You are by a better sea
You have the best rivers
You’re a good ease

You are when you are nice
You have good animals
You have a good mountains
Your Children are Completely Fight

A candidate when I’m kneeling down
Worship the Creator of heaven
Please do not master the world punish punish me as a parent
Oh my god

Yah-yah, yah
(Mother Malawi)
(Mother Malawi)
Seven of achina adah

(Mother Malawi)
(Mother Malawi)
(No-no-no-no, no-no-no-no-no)
(No-no-no-no, no-no-no-no-no)
Find more lyrics at https://dcslyrics.com

SevenOmore Lyrics – My Malawi

Please support our site by sharing it.
And please follow our site to get the latest lyrics for all your favourite songs.

Please support the artist and us by purchasing your favourite music thru our Amazon Music and Apple Music links 🙂

You can purchase their music thru
DCSLyrics.com Amazon Music    DCSLyrics.com Apple Music
Disclosure: As an Amazon Associate and an Apple Partner, we earn from qualifying purchases

From the album:
My Malawi
Release Year: 2022